Apolisi ya Nathenje m’boma la Lilongwe amanga a Luwashi Bakali, 26, powaganizira kuti apha mwana omupeza wazaka ziwiri. Izi zachitika m’mudzi wa Kawale kwa mfumu...
Ophunzira pa sukulu yaukachenjede ya University of Malawi(Unima) ku Zomba akhazikitsa chipangizo chothandiza anthu omwe ali ndi ulumali wosaona. Mmodzi mwa ophunzirawo, Hudson Mwangalika, wati...
Chileka Police Station has urged learners at Lipunga Primary School in Blanytre to work hard so that they become reliable future citizens. Led by Superintendent...
South West Police Region has commended the business community in the region for supporting them in strengthening security ahead of the festive season. Commissioner of...
Anthu a midzi ya Mphampha ndi Tsambalabooka kwa mfumu yaikulu Lundu ku Chikwawa ati ndi okondwa kuti tsopano adzimwa madzi aukhondo. Anthuwa anena izi kampani...
Apolisi munzinda wa Zomba amanga a Jessie Mpanira, 35, powaganizira kuti amafuna kulowetsa chamba ku ndende ya Zomba Maximum. Wachiwiri kwa ofalitsa nkhani za polisi...
Department of Climate Change and Meteorological Services (MET) has forecast erratic rainfall in Blantyre this month, with continuous normal to above-normal rainfall expected to begin...
Apolisi ku Chikwawa akufunafuna ophunzira omwe aphwanya ofesi ya mphunzitsi wamkulu pasukulu ya pulaimale ya Mitondo m’bomalo ati poganiza kuti mphunzitsi wamkuluyo akuchita zinthu za...
Scotland Police is delivering a two-week training on human rights protection to facilitators at the Malawi Police Service, as a long-standing partnership between Malawi and...