Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

A Nankhumwa akhazikitsa chipani

Mtsogoleri wa chipani chatsopano cha People’s Development (PDP), Kondwani Nankhumwa, wati chipanichi chabwera kudzasintha Malawi kukhala dziko lodzidalira pa chakudya, la umodzi ndinso kulimbikira pantchito.

Poyankhula pamsonkhano wa atolankhani mumzinda wa Blantyre, iwo ati chipanichi chithetsa m’chitidwe okakamira m’maudindo muzipani.

A Nankhumwa atinso a Malawi akufunika chipani chomwe chingamalore anthu kupikisana momasuka.

Wolemba: Blessings Cheleuka

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

National Bank yapanga phindu lokwana K71.96 billion chaka chatha

Justin Mkweu

Mbali ina ya msewu wa Chiwembe sanamange bwino — Chimwendo Banda

MBC Online

PROPHET SHEPHERD BUSHIRI AGAWA CHIMANGA M’MABOMA AKUM’MWERA KUMAPETO ASABATAYI

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.