Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local News Nkhani Tourism

Sitima yapakati pa LL, BT iyambanso kuyenda — Hara

Nduna yaza mtengatenga, a Jacob Hara, yati sitima yoyenda pakati pa mizinda ya Blantyre ndi Lilongwe iyambiranso posachedwapa.

A Hara anati gawo lachiwiri ikhala kukonzanso njanji yolowera m’boma la Mchinji pofuna kulumikizitsana ndi dziko la Zambia.

Iwo ati izi zili chomwechi chifukwa akonza mlatho omwe unaduka zomwe zichititse kuti sitima iyambenso kuyenda.

Olemba : Patrick Dambula

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Nearly 70 percent of children in Malawi multi-dimensionally poor – Report

MBC Online

World Bank appoints Firas Raad as Malawi’s Country Manager

Romeo Umali

Two remanded men charged with murder

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.