Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local News Nkhani Tourism

Sitima yapakati pa LL, BT iyambanso kuyenda — Hara

Nduna yaza mtengatenga, a Jacob Hara, yati sitima yoyenda pakati pa mizinda ya Blantyre ndi Lilongwe iyambiranso posachedwapa.

A Hara anati gawo lachiwiri ikhala kukonzanso njanji yolowera m’boma la Mchinji pofuna kulumikizitsana ndi dziko la Zambia.

Iwo ati izi zili chomwechi chifukwa akonza mlatho omwe unaduka zomwe zichititse kuti sitima iyambenso kuyenda.

Olemba : Patrick Dambula

Related posts

‘Government grants will boost ATM Strategy’

Rabson Kondowe

Green Climate Fund approves $52.3 million for Malawi

Blessings Kanache

Let’s pray for one another — Usi

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.