Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Ndatula pansi udindo wa utsogoleri wa aphungu otsutsa boma — Nankhumwa

Yemwe anali mtsogoleri wa aphungu otsutsa boma ku nyumba ya malamulo, Kondwani Nankhumwa, walengeza kuti watula pansi udindowu.

Iwo ati zikhala zovuta kupitilirabe kukhala pa udindowu pambuyo poyambitsa chipani chawo chatsopano.

Poyankhula munzinda wa Blantyre, iwo ati pakali pano awuza kale owaimira pa mlandu okhudza ofesiyi omwe uli ku bwalo lamilandu kuti awuyimitse.

Olemba: Blessings Cheleuka

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

‘Pokhala pabwino ndipofunika msukulu’

MBC Online

Boma lipitiriza kumamvana ndi ma Bishopu a Katolika

Blessings Kanache

Unduna oona za madzi wati upitilira kupereka madzi abwino

Beatrice Mwape
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.