Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Ndatula pansi udindo wa utsogoleri wa aphungu otsutsa boma — Nankhumwa

Yemwe anali mtsogoleri wa aphungu otsutsa boma ku nyumba ya malamulo, Kondwani Nankhumwa, walengeza kuti watula pansi udindowu.

Iwo ati zikhala zovuta kupitilirabe kukhala pa udindowu pambuyo poyambitsa chipani chawo chatsopano.

Poyankhula munzinda wa Blantyre, iwo ati pakali pano awuza kale owaimira pa mlandu okhudza ofesiyi omwe uli ku bwalo lamilandu kuti awuyimitse.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

‘Pewani kufalitsa nkhani zabodza’

Romeo Umali

Owona zaumoyo atulutsa zotsatira zonse za ‘ambuye tengeni’ mu sabata ziwiri

MBC Online

Azimayi sakugwiritsa ntchito makondomu achizimayi

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.