Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Mbali ina ya msewu wa Chiwembe sanamange bwino — Chimwendo Banda

Nduna yoona za maboma aang’ono komanso umodzi ndi chikhalidwe, a Richard Chimwendo Banda, yati siyokhutitsidwa ndi m’mene gawo lina la msewu wa Chiwembe mu mzinda wa Blantyre awumangira.

Iyo imanena izi itayendera misewu yamadulira imene akuimanga mu mzindawu, ndipo iwo ati nkhaniyi asiyira akuluakulu oona za mamangidwewa.

Komabe, a Chimwendo Banda ati ndi okondwa kuti miseu yambiri yamangidwa bwino.

Olemba : Blessings Cheleuka

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Entrepreneurial breakthrough is digital — Graça Machel Trust, COMFWB

Aisha Amidu

LL Police nabs TikToker for suspected fraud

Romeo Umali

BT to host Kamuzu Day celebrations

Eunice Ndhlovu
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.