Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Mbali ina ya msewu wa Chiwembe sanamange bwino — Chimwendo Banda

Nduna yoona za maboma aang’ono komanso umodzi ndi chikhalidwe, a Richard Chimwendo Banda, yati siyokhutitsidwa ndi m’mene gawo lina la msewu wa Chiwembe mu mzinda wa Blantyre awumangira.

Iyo imanena izi itayendera misewu yamadulira imene akuimanga mu mzindawu, ndipo iwo ati nkhaniyi asiyira akuluakulu oona za mamangidwewa.

Komabe, a Chimwendo Banda ati ndi okondwa kuti miseu yambiri yamangidwa bwino.

Olemba : Blessings Cheleuka

Related posts

Parliament impressed by FDH’s corporate responsibility

MBC Online

Unofficial results: MCP wins all three wards

Romeo Umali

NGORA records 54% compliance rate

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.