Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Ochita malonda achita zionetsero ku Lilongwe

Ochita malonda a zovala zakaunjika mu mnzinda wa Lilongwe akuchita zionetsero kamba kakukwera kwa misonkho pa mabelo a zovalazi.

Pakali pano, ochita malondawa afika pa ofesi ya bungwe lotolera misonkho ya Malawi Revenue Authority (MRA) komwe akudzatula zikalata zawo zamadandaulo.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Loya amangidwa pomuganizira kuti ali ndi galimoto yobedwa

Mayeso Chikhadzula

WOMAN JAILED 5 YEARS FOR WOUNDING STEPDAUGHTER

MBC Online

ADRA BACKS DISASTER BILL

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.