Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Ochita malonda achita zionetsero ku Lilongwe

Ochita malonda a zovala zakaunjika mu mnzinda wa Lilongwe akuchita zionetsero kamba kakukwera kwa misonkho pa mabelo a zovalazi.

Pakali pano, ochita malondawa afika pa ofesi ya bungwe lotolera misonkho ya Malawi Revenue Authority (MRA) komwe akudzatula zikalata zawo zamadandaulo.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Airtel Malawi Introduces Combo Bundle

McDonald Chiwayula

Kuchedwa kwa nsewu wa Ilomba kwadandaulitsa boma

MBC Online

LL POLICE NABS 5 IN CONNECTION WITH ALLEGED ROBBERY

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.