Category : Nkhani
Msonkhano waukulu tichita mu September — JB
Prezidenti wa chipani Cha PP, Dr Joyce Banda walengeza kuti chipanichi chidzakhala ndi msonkhano wake waukulu pa 7 September chaka chino mumzinda wa Lilongwe. Iwo...
Nancholi yayankhula
Kuli khwimbi la undipondera mwana pa bwalo la Nancholi mu mzinda wa Blantyre pamene mtsogoleri wakale wa dziko llino Dr Joyce Banda akuchititsa msonkhano. A...
A Dossi ayikidwa m’manda ndi mwambo wachisilikali
Mwambo oyika m’manda malemu Moses Dossi, omwe anaakhalapo olembankhani za masewero komanso nduna ya zamasewero mu ulamulo wa boma la chipani cha United Democratic Front,...
‘Tidziyamba ndife aMalawi kutsatsa malonda a dziko lathu’
Mtsogoleri wadziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wati dziko lino silikuchita bwino kwenikweni chifukwa choti timataya nthawi ndikufalitsa zinthu zoononga mbiri yathu m’malo mofalitsa zambiri zabwino...
‘Malo nawa koma tionepo chitukuko pasanathe zaka ziwiri’
Mwambo opereka malo kwa atsikana osewera mpira wa miyendo mutimu ya Scorchers wayamba ndi kupereka zikalata zaumwini kwa osewerawa ku unduna wa zamalo ku Lilongwe,...
Scorchers lero imwemwetera
Atsikana amene amasewera mpira wamiyendo mu timu yadziko lino ya Scorchers adzuka ndinkhope zowala chifukwa lero boma likuyembekezeka kukwaniritsa zimene mtsogoleri wadziko lino, Dr Lazarus...
Ntchito yojambula msewu wa Makanjira-Mangochi igwiridwa mwachangu
A Saudi Fund for Development ati afulumizitsa ntchito yojambula msewu wa Makanjira ku Mangochi kuti ntchito yomanga msewuwu iyambe mwachangu. Izi akuti zikutengera chidwi chomwe...
Awamanga powaganizira kuti amafuna kulowetsa chamba ku ndende
Apolisi ku Zomba amanga Estery Evance wazaka 19 ndi Bonface Phiri wazaka 22 powaganizira kuti amafuna kulowetsa chamba ku ndende yaikulu ya Zomba. Ofalitsankhani wapolisi...

