Adindo a malo ochitira kafukufuku a Chitedze Research Station ku Lilongwe adandaula ndi mchitidwe wodula mitengo omwe akuti ukusokoneza ntchito zina za kafukufuku pa malopa....
Bungwe la Mulakho wa a Lhomwe lati ndi lodabwa ndi mafumu ena omwe sakumvetsa zakusankha kwa mfumu yatsopano ya a Lhomwe Paramount Chief Kaduya. Wapampando...
Bungwe la Malawi Gaming and Lotteries Authority ( MAGLA), lachenjeza kuti lamulo ligwira ntchito kwa makolo omwe amalimbikitsa ana awo kuchita juga. Mkulu wa bungwe...