Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Politics

Nancholi yayankhula

Kuli khwimbi la undipondera mwana pa bwalo la Nancholi mu mzinda wa Blantyre pamene mtsogoleri wakale wa dziko llino Dr Joyce Banda akuchititsa msonkhano.

A George Nnesa, omwe ndi mtsogoleri wa chipani cha Mafunde, nawo alinso pa msonkhanowu.

Padakali pano, a Noah Chimpeni ndi amene akuchita zoyankhula pamene akulandila akulu akulu amene anali ku chipani chotsutsa cha DPP ku chipani cha PP.

Olemba : Blessings Cheleuka

#MBCDigital
#Manthu

Related posts

World Bank lauds Chikwawa District Council

Romeo Umali

Tambala Super Cup unveiled in Blantyre

Romeo Umali

Ministry of Gender lauds Ecobank for promoting e-payments

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.