Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

A Dossi ayikidwa m’manda ndi mwambo wachisilikali

Mwambo oyika m’manda malemu Moses Dossi, omwe anaakhalapo olembankhani za masewero komanso nduna ya zamasewero mu ulamulo wa boma la chipani cha United Democratic Front, uli mkati m’mudzi mwa Kalimanjera kwa Chapananga m’boma la Chikwawa.

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, walamula kuti malemu Dosi ayikidwe m’manda motsatira mwambo wa chisilikali popereka ulemu ku ntchito zawo.

Nduna yoona zamalo, a Deus Gumba, ndi amene akuyimilira prezidenti wa dziko lino.

A Dossi anamwalira lachinayi mmawa atadwala kwa nthawi yayitali.

Related posts

NGORA yati K1BN ithandiza mabungwe awo kudzidalira

Romeo Umali

“Osanyoza anthu achikulire” — Chakwera

Romeo Umali

DoDMA ifikira aliyense

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.