Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Politics

Msonkhano waukulu tichita mu September — JB

Prezidenti wa chipani Cha PP, Dr Joyce Banda walengeza kuti chipanichi chidzakhala ndi msonkhano wake waukulu pa 7 September chaka chino mumzinda wa Lilongwe.

Iwo alengeza izi ku Nancholi komwe anachititsa msonkhano wandale.

Iwo ati ndi okondwa kuti chipani cha PP ndi champhamvu ku Blantyre ndipo apempha owatsatira kuti apitirize kusunga bata.

Khwimbi la anthu linasonkhana kumsonkhanowu pabwalo la Nancholi ndipo nawo aGeorge Nnesa, mtsogoleri wa chipani Cha Mafunde, analinso nawo pa msonkhanowu.

Olemba: Blessings Cheleuka
#MBCDigital
#Manthu

Related posts

Police officer donates school uniform in Lilongwe

Romeo Umali

Masomphenya group offers support to Karonga’s vulnerable

Rabson Kondowe

AMEA POWER TO INSTALL 50 MEGAWATTS FACILITY

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.