M’busa wa mpingo wa Synagogue Pentecostal Church Prophet Millward Nyangulu wapereka thandizo la matumba a chimanga 200 komanso ndalama zokwana K6 million ku Home of...
Phungu wadera la Mangochi-Makanjira a Benedicto Chambo ati iwo ndi anthu amdera lao lomwe ndi kumpoto kwa boma la Mangochi alipambuyo pa boma la Malawi...
Kukhala nkoke-nkoke pakati pa matimu mu mpikisano wa Champion Kabvina chaka chino pomwe ndalama zomwe matimu amalimbirana zakwera kuchoka pa K13 miliyoni kufika pa K20...
Mtsogoleri wa dziko lino, Dr. Lazarus Chakwera, wati chipata cha Mwanza ndi chofunika kuti kuzikhala malonda zomwe zingathe kubweretsa chitukuko m’Bomali. Chipata-chi ndi chatsopano ndipo...
Gulu la achinyamata a chipani cha Malawi Congress lotchedwa MCP Youth League lapereka katundu osiyana siyana kwa odwala mu chipinda chochilira amai pachipatala chaching’ono cha...
Boma lathetsa mulandu wa anthu atatu omwe anawamanga chifukwa chosokoneza mdipiti wa mtsogoleri wa dziko lino pa HHI mu mzinda wa Blantyre. Mkulu oimira boma...