Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akawonekera ku nyumba ya malamulo ndikukayankha mafunso kuchokera kwa aphungu anyumbayi. Potsimikiza izi, mneneri wa Boma, a...
Mtsogoleri wa dziko lino Dr. Lazarus Chakwera wasankha a Jacob Mazalale ngati mlembi mu unduna wa zachuma oona za mapulani achitukuko. A Mazalale, amene ndi...
Nduna ya zofalitsa nkhani yemwenso ndi m’neneri wa boma, a Moses Kunkuyu, ati mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera watsindika kuti palibe munthu amene...
Bwalo la Magistrate mumzinda wa Lilongwe lagamula kuti nzika zitatu zadziko la China zikakhale mndende kwa zaka zisanu ndi chimodzi atazipeza olakwa pa mlandu ozembetsa...
Bank ya NBS yathandiza anthu okalamba komanso a ulumali ndi matumba a ufa wa chimanga kummwera kwa boma la Chiradzulu. Poyankhula popereka thandizoli, mkulu wa...
Nduna yoona za chilengedwe ndi kusintha kwa nyengo, Dr Michael Usi, yalangiza a Malawi kuti adzitha kumafunsa mafunso atsogoleri awo mmalo momangodandaula akaona kuti zinthu...
Ntchito yogawa chimanga chaulere kwa anthu ovutika yomwe akuchita mtsogoleri wa mpingo wa Enlightened Christian Gathering the Jesus Nation Prophet Shepherd Bushiri ipitilira nchigawo chakummwera...
Mnyamata wa zaka 20 wa ku Lilongwe, wapeza mphoto ya ndalama zokwana K174.2 million atasewera masewero oulutsa ndege ndi BetPawa. Akuluakulu a kampaniyi atsimikiza izi...