Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

President Chakwera awonekera m’nyumba ya malamulo

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akawonekera ku nyumba ya malamulo ndikukayankha mafunso kuchokera kwa aphungu anyumbayi.

Potsimikiza izi, mneneri wa Boma, a Moses Kunkuyu, wati President Chakwera akawonekera ku nyumbayi pokwaniritsa malonjezo ake woti adzakhala wotumikira anthu a m’dziko muno poyankha mafunso kudzera kwa aphungu awo.

Mtsogoleri wadziko linoyu akakhala ali ku nyumba ya malamulo masana ano kuyambira nthawi ya 2 koloko.

Wolemba: Timothy Kateta

#MBCOnlineServices

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Match-fixing case awaits consent from the DPP

MBC Online

Alipire chindapusa chifukwa chotchula mzake kuti mfiti

MBC Online

Karonga District Council cracks whip on uncomplying mill operators

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.