Mkulu wa bungwe lophunzitsa ntchito za luso la manja la Technical Entrepreneur and Vocational Education and Training Authoritiy (TEVETA), a Elwin Sichiola, alimbikitsa achinyamata amene...
Kafukufuku yemwe bungwe la amalonda la Malawi Confederation of Chambers of Commerce and Industry (MCCCI) lachita waonetsa kuti kampani 50 mwa 100 zilizonse m’dziko muno...
Timu ya Silver Strikers yasayina amene anali osewera kutsogolo kwa timu ya Dedza Dynamos, Charles Chipala, pa mgwirizano wa zaka zitatu. Chipala wasewereraponso matimu monga...
Kuli mpungwepungwe ku nyumba ya malamulo pomwe zokambirana kunyumbayi zayamba ndipo a Kondwani Nankhumwa komanso a Mary Navicha anaimilira ngati mtsogoleri wa zipani zotsutsa. Awiriwa...
Mmodzi wa akulu akulu mchipani cha MCP yemwenso ndi nduna yaza Chitetezo Chadziko a Ken Zikhale Ng’oma ati boma lipitiriza kutukula madera onse a dziko...
Nduna ya maboma ang’ono a Richard Chimwemdo Banda yalangiza mafumu kuti adzionetsetsa kuti pali chilungamo pothandiza anthu a m’midzi. A Chimwendo Banda omwenso ndi...
Membala watsopano wachipani cha Malawi Congress (MCP) a Uladi Mussa athokoza mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera chifukwa chokhulukira milandu yawo ndi ya mtsogoleli...
Timu ya Silver Strikers yalemba ntchito Peter Mponda ngati mphunzitsi wa timuyi amene akulowa m’malo mwa Pieter De Jongh yemwe adatula pansi udindo wake mwezi...