Malawi Broadcasting Corporation
Health Local Local News Nkhani

Azimayi sakugwiritsa ntchito makondomu achizimayi

Zadziwika kuti amayi ambiri sakonda kugwiritsa ntchito makondomu achizimayi zomwe zikupangitsa kuti makondomu-wa adziwonongeka asanagwiritsidwe ntchito.

Wanena izi ndi mkulu owona zopewa kufala kwa kachirombo ka HIV wa bungwe la Aids Healthcare Foundation (AHF) kuchigawo chakum’mwera, a Jacob Pidini.

Iwo amafotokoza izi pamwambo wa tsiku lokumbukira kufunika kwa kondomu popewa kutenga mimba zosayembekezera, kutenga matenda opatsirana pogonana kuphatikizapo HIV.

 

Related posts

ESCOM, MEAP project to connect over 90,000 customers by June

Rabson Kondowe

Mayi wathawa atatentha manja a mwana wake

Alinafe Mlamba

Four arrested for possession of forest produce without permit

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.