Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Tipitiriza kuthandiza – NBS Bank

Bank ya NBS yathandiza anthu okalamba komanso a ulumali ndi matumba a ufa wa chimanga kummwera kwa boma la Chiradzulu.

Poyankhula popereka thandizoli, mkulu wa Branch ya Limbe, a Twaibu Nnani, ati bankiyi ipitiriza kuthandiza osowa kudzera mu njira zosiyanasiyana.

Ndipo mfumu yaikulu Mpunga yapempha mabungwe akufuna kwabwino kuti athandize mabanja omwe akhudzidwa ndi njala.

Malinga ndi a Mpunga thandizoli ati ndi lapafupifupi K3.5 million.

Wolemba: Blessings Cheleuka

 

Related posts

Dr Chakwera achita zokambilana zobweretsa sitima zapamadzi

Blessings Kanache

Usi atsekulira msonkhano okambirana za magetsi

Romeo Umali

Anyamata awiri anjatidwa ataba katundu wa K500,000

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.