Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

MNENERI BUSHIRI WAGAWA CHIMANGA KU THYOLO

Prophet Shepherd Bushiri wagawa chimanga kwa Nchilamwera m’boma la Thyolo komwe wapempha anthu kuti asalowetse ndale pa thandizo lake.

Mneneri Bushiri wati apitirizabe kupereka chimanga kwa anthu okhudzika ndi njala m’madera onse m’dziko muno, pomwe mabanja oposa 40,000 tsopano alandira chimangacho.

Mneneriyu wapemphanso amfumu a Nchilamwera kuti adziwitse a khonsolo ya bomali kuti ngati angamulole, athandize pantchito yomanga technical college pa boma la Thyolo.

 

Related posts

Ansah wants speedy development of Nacala Corridor

Romeo Umali

FDH hikes Mayors’ Trophy sponsorship to K100 million

Romeo Umali

Mayi Monica Chakwera atsogolera amayi pa mapemphero a tsiku la a mayi

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.