Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

MNENERI BUSHIRI WAGAWA CHIMANGA KU THYOLO

Prophet Shepherd Bushiri wagawa chimanga kwa Nchilamwera m’boma la Thyolo komwe wapempha anthu kuti asalowetse ndale pa thandizo lake.

Mneneri Bushiri wati apitirizabe kupereka chimanga kwa anthu okhudzika ndi njala m’madera onse m’dziko muno, pomwe mabanja oposa 40,000 tsopano alandira chimangacho.

Mneneriyu wapemphanso amfumu a Nchilamwera kuti adziwitse a khonsolo ya bomali kuti ngati angamulole, athandize pantchito yomanga technical college pa boma la Thyolo.

 

Related posts

Chibuku supports Queens with K2 million

Rabson Kondowe

Chakwera to launch construction of cost-effective classroom blocks

Romeo Umali

Solar projects bring clean water, electricity to Malawians

Doreen Sonani
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.