Malawi Broadcasting Corporation
News

President Chakwera wafika ku Lilongwe kuchokera ku Blantyre

President wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera wafika ku Lilongwe, kuchokera ku Blantyre komwe anapita kukatsekulira chionetsero chazamalonda.

Pofika pa bwalo la ndege la Kamuzu International ku Lilongwe, President Chakwera analandiridwa ndi Mlembi wamkulu mu ofesi ya prezidenti ndi nduna zake, a Colleen Zamba ndi akuluakulu ena.

Dr Chakwera anaoneranso magule amene anavina amayi a zipani za Malawi Congress ndi UTM.


Olemba: Isaac Jali

Related posts

Man arrested for alleged murder in Nkhata Bay

Romeo Umali

Carbon credit hidden treasure for Malawi – financial expert

Rabson Kondowe

Disaster reporting drill excites journalists

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.