Malawi Broadcasting Corporation
News

President Chakwera wafika ku Lilongwe kuchokera ku Blantyre

President wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera wafika ku Lilongwe, kuchokera ku Blantyre komwe anapita kukatsekulira chionetsero chazamalonda.

Pofika pa bwalo la ndege la Kamuzu International ku Lilongwe, President Chakwera analandiridwa ndi Mlembi wamkulu mu ofesi ya prezidenti ndi nduna zake, a Colleen Zamba ndi akuluakulu ena.

Dr Chakwera anaoneranso magule amene anavina amayi a zipani za Malawi Congress ndi UTM.


Olemba: Isaac Jali

Related posts

14 to benefit from Mpinganjira’s business capital project

Rabson Kondowe

NOCMA optimistic of continued stable fuel supply

Romeo Umali

Veep assures disaster-affected communities of govt support

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.