Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Dr Chakwera wabwelera ku Lilongwe

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wanyamuka ku Blantyre kubwelera ku Lilongwe atatsekulira chionetsero chazamalonda ku Chichiri Trade Fair grounds.

Wapampando wa chipani cha MCP m’chigawo chakummwera, a Peter Simbi, akuluakulu ena aboma komanso atsogoleri andale ndi mafumu ndi ena mwa omwe anapelekeza Dr Chakwera komanso First Lady Madam Monica Chakwera pabwalo la ndege la Chileka.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

SACCOs key to economic growth — Itaye

MBC Online

MERA doubles fuel supply procurement to control crisis

Steve Dakalira

Osalowetsa ndale pofuna kutchuka pa maliro- Joe thomas Nyirongo

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.