Category : Nkhani
Temwa aveka makanda pa chipatala cha Kamuzu Central
Katswiri oyimba nyimbo za Amapiano, Temwa, wati iye ndi odzipereka kuthandiza ana osowa amene agonekedwa mu zipatala m’dziko muno. Temwa amayankhula izi pa chipatala cha...
Dr Usi ati adzipereka pofuna kukweza miyoyo ya a Malawi
Wachiwiri watsopano kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, wati adzipereka kwathunthu kuthandiza Prezidenti Dr Lazarus Chakwera potukula dziko lino komanso kukweza aMalawi. Iwo...
Anthu ena akuonera nawo mwambo panja pa nyumba ya malamulo
Anthu ena alipanja pa nyumba ya malamulo pomwe ayika kanema pofuna kupereka mwayi kwa anthuwo oonelera mwambo wolumbilitsa Dr Michael Bizwick Usi kukhala wachiwiri kwa...
Nkhani sindalama koma zomwe Bullets yachita – Silver Strikers
Mkulu wa timu ya Silver Strikers Patrick Chimimba wati chidwi chikhale pa zomwe Bullets yachita povomereza ndikupepesa ku timu ya Silver osati ndalama zomwe apereka....
Wapampando wa MEC alumbiritsidwa lachisanu
Wapampando watsopano wa bungwe loyendetsa zisankho la MEC, Justice Annabel Mtalimanja, alumbilitsidwa lachisanu pa 21 June, 2024 ku Lilongwe High court nthawi ya 9 koloko...
Kusankhidwa kwa Justice Mtalimanja kulimbikitsa atsikana, amayi — Undule
Katswiri pa utsogoleri ndi ufulu wa anthu, a Undule Mwakasungula, ati kusankhidwa kwa Justice Annabel Mtalimanja ngati wapampando wa bungwe la MEC ndi chilimbikitso kwa...
Admarc idzigula chimanga pamtengo okwera
Bungwe la Admarc tsopano lidzigula chimanga pa mtengo wa K700 pa kilogramme (K35,000 pa thumba la 50 kilogrammes), malinga ndi mkulu wa bungweli, a Daniel...
Mayi amangidwa poganiziridwa kuti wapha mwamuna wake
Apolisi ku Lilongwe amanga a Ruth Nkhoma powaganizira kuti anapha amuna awo a Misheck Bayison powakoka ndi kupotokola ziwalo zobisika kaamba kakusamvana pa ndalama yokwana...

