Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Health Local News Nkhani

Temwa aveka makanda pa chipatala cha Kamuzu Central

Katswiri oyimba nyimbo za Amapiano, Temwa, wati iye ndi odzipereka kuthandiza ana osowa amene agonekedwa mu zipatala m’dziko muno.

Temwa amayankhula izi pa chipatala cha Kamuzu Central munzinda wa Lilongwe pamene amapereka zovala za mphepo ndi zina kwa ana omwe agonekedwa pa chipatalachi.

Iye wati thandizo lina lomwe ndi la ndalama zokwana K1million lachokera kwa anthu akufuna kwabwino.

Sabata ya mawa, Temwa akhala akugawa zovala kwa ophunzira osowa pa sukulu ya pulayimale ya Kalambo ku Area 25 mu mzinda wa Lilongwe.

 

Related posts

Capital Hill to help smallholder farmers unlock markets

Romeo Umali

NRB extends phase 7 of National ID and Death Certificate registration

Romeo Umali

Christian organisation hands over 30 houses to the elderly

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.