Malawi Broadcasting Corporation
Development Health Local News Nkhani

Achinyamata awapempha kuti athandize boma pa chitukuko

Bungwe la Chiwalo Youth Network lalangiza achinyamata a m’boma la Phalombe kuti athandize kulimbikitsa ukhondo m’makomo mwawo komanso m’malo a boma monga ku Polisi ndi ku chipatala.

Wapampando wa bungweli, a Patrick Makwale, ndi amene ananena izi pamene achinyamata ena amagwira ntchito yosesa pa chipatala cha boma cha Nambazo komanso Polisi ya Nambazo m’bomalo.

A Makwale anati ndi okondwa poona kuti achinyamata ambiri ku Phalombe akuonetsa chidwi pa ntchiito za chitukuko, potukula miyoyo yawo komanso ntchito za boma.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

‘Research, Innovation key to development’

MBC Online

MODERN POST-HARVEST HANDLING METHOD REDUCING LOSSES

MBC Online

MIA ENERGISES 16-YEAR-OLD ENVIRONMENTALIST WITH K.5 MN

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.