Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Business Development Local Local Nkhani

Admarc idzigula chimanga pamtengo okwera

Bungwe la Admarc tsopano lidzigula chimanga pa mtengo wa K700 pa kilogramme (K35,000 pa thumba la 50 kilogrammes), malinga ndi mkulu wa bungweli, a Daniel Makata.

Mtengowu wakwera kuchoka pa K650 pa kilogramme (K32,500 pa thumba lolemera 50 kilogrammes) umene boma linakhazikitsa ngati poyambira.

A Makata ati Admarc yachita izi pofuna kuwonetsetsa kuti alimi akupindula ndi ulimi monga boma likufunira.

 

Related posts

Actallliance launches El Niño Response in Lower Shire

Romeo Umali

Alimi asamale pogula mbewu — Self Help Africa

Romeo Umali

Govt to launch MCA Land Productivity Project next week

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.