Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Kusankhidwa kwa Justice Mtalimanja kulimbikitsa atsikana, amayi — Undule

Katswiri pa utsogoleri ndi ufulu wa anthu, a Undule Mwakasungula, ati kusankhidwa kwa Justice Annabel Mtalimanja ngati wapampando wa bungwe la MEC ndi chilimbikitso kwa amai ndi atsikana m’dziko muno.

A Mwakasungula ati izi zawonetsa chidwi cha mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera chokweza amayi m’maudindo osiyanasiyana.

Justice Annabel Mtalimanja awasankha kulowa mmalo mwa Justice Dr. Chifundo Kachale omwe nthawi yawo yogwira ntchito pa mpandowu yatha.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

Thupi la Dr Chilima aliyika m’manda

Mayeso Chikhadzula

South West Region records drop in crime rate

Alinafe Mlamba

Tertiary institution urges private sector to support needy students

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.