Phungu wadera la pakati munzinda wa Lilongwe wayamika boma kaamba ka ntchito zachitukuko zomwe likugwira mdera lawo. Phunguyi, a Alfred Jiya, wati boma lawamangira misewu...
Mkulu oyang’anira ndale ku chipani cha Malawi Congress (MCP), a Maxwell Thyolera, ati ndale zoopsyeza ena, zimene anati akupanga a zipani zina ndi zosaloredwa mu...
Ligi ya masewero a Darts m’chigawo chapakati yalandira K6 million imene yachokera ku kampani yogulitsa zipangizo zaulimi ndi mankhwala ya SKM trading imenenso asayinirana nayo...
Dera la mfumu yaikulu Chiseka m’boma la Lilongwe lakwanitsa kuchotsa ana okwana 169 ku mabanja a ana kuyambira mu chaka cha 2023 kufikira pano, adindo...
Nduna ya zaumoyo, a Khumbize Kandodo Chiponda, yapempha anthu m’dziko muno kuti apewe m’chitidwe wa katangale ndi ziphuphu pofuna kupeza ndi kupereka thandizo la zaumoyo...
Apolisi ku Mangochi amanga Dalitso Nkutu, 19, pomuganizira kuti wabaya ndi mpeni bwenzi lake amene amamuganizira kuti akuzemberana ndi amuna ena. Mneneri wa polisi ku...
Bungwe la Green Girls Club lapempha unduna wa za achinyamata kuti uyike njira zoteteza atsikana pa nthawi imene kwagwa ngozi zadzidzidzi, maka zakudza kaamba ka...
Apolisi m’boma la Balaka adandaula ndi kukwera kwa chiwerengero cha milandu yokhuza nkhanza m’mawanja m’bomalo. Malinga ndi wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo, a Gladson M’bumpha,...