Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Ana 169 apulumutsidwa ku maukwati

Dera la mfumu yaikulu Chiseka m’boma la Lilongwe lakwanitsa kuchotsa ana okwana 169 ku mabanja a ana kuyambira mu chaka cha 2023 kufikira pano, adindo atero.

Oyang’anira achinyamata m’derali, a Chimwemwe Diliwo, ndi amene anena izi ku Lilongwe pa msokhano umene bungwe la ArtGlo likuchititsa m’bomali omwe ukulimbana ndi nkhanza zimene ana akukumana nazo.

Iwo ati nkhanza zosiyanasiyana zikuchepa mderalo kaamba ka upangiri wamphamvu.

Olemba: Lonjezo Msodoka

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Silver Strikers clinch TNM Super League title

Romeo Umali

ESCOM set to offer internet services

Rabson Kondowe

Mozambique-Malawi project ready by 2025 – ESCOM

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.