Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Ana 169 apulumutsidwa ku maukwati

Dera la mfumu yaikulu Chiseka m’boma la Lilongwe lakwanitsa kuchotsa ana okwana 169 ku mabanja a ana kuyambira mu chaka cha 2023 kufikira pano, adindo atero.

Oyang’anira achinyamata m’derali, a Chimwemwe Diliwo, ndi amene anena izi ku Lilongwe pa msokhano umene bungwe la ArtGlo likuchititsa m’bomali omwe ukulimbana ndi nkhanza zimene ana akukumana nazo.

Iwo ati nkhanza zosiyanasiyana zikuchepa mderalo kaamba ka upangiri wamphamvu.

Olemba: Lonjezo Msodoka

Related posts

SAFEGUARD PUBLIC FUNDS, CHIMWENDO PLEADS WITH COUNCILS

Rabson Kondowe

Peter Mgangira: The quiet architect of Silver Strikers’ return to glory

Rabson Kondowe

US Army Maps Malawi to Aid Government’s Decision-Making

Yamikani Simtowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.