Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Ana 169 apulumutsidwa ku maukwati

Dera la mfumu yaikulu Chiseka m’boma la Lilongwe lakwanitsa kuchotsa ana okwana 169 ku mabanja a ana kuyambira mu chaka cha 2023 kufikira pano, adindo atero.

Oyang’anira achinyamata m’derali, a Chimwemwe Diliwo, ndi amene anena izi ku Lilongwe pa msokhano umene bungwe la ArtGlo likuchititsa m’bomali omwe ukulimbana ndi nkhanza zimene ana akukumana nazo.

Iwo ati nkhanza zosiyanasiyana zikuchepa mderalo kaamba ka upangiri wamphamvu.

Olemba: Lonjezo Msodoka

Related posts

UTM supporters flock to welcome Usi in Mzuzu

MBC Online

MRA drone border patrols to save billions

Rabson Kondowe

Commentators agitate for bank notes replacement to punish looters

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.