Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Ana 169 apulumutsidwa ku maukwati

Dera la mfumu yaikulu Chiseka m’boma la Lilongwe lakwanitsa kuchotsa ana okwana 169 ku mabanja a ana kuyambira mu chaka cha 2023 kufikira pano, adindo atero.

Oyang’anira achinyamata m’derali, a Chimwemwe Diliwo, ndi amene anena izi ku Lilongwe pa msokhano umene bungwe la ArtGlo likuchititsa m’bomali omwe ukulimbana ndi nkhanza zimene ana akukumana nazo.

Iwo ati nkhanza zosiyanasiyana zikuchepa mderalo kaamba ka upangiri wamphamvu.

Olemba: Lonjezo Msodoka

Related posts

Govt to boost SME economic transformation

Romeo Umali

Dept of Immigration to resume passport printing

Rabson Kondowe

OXFAM yaika padera K650m yothandizira amayi pandale

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.