Category : Nkhani
MCP ipitiriza kukwaniritsa malonjezo — Kabwila
Chipani cha Malawi Congress (MCP) chati sichichita nawo ndale zoononga, zodana komanso zolozana zala ndipo m’malo mwake chipitiriza kugwira ntchito za chitukuko zolozeka zimene zitasinthe...
Burning Spear wapereka mphatso ya gitala kwa President Chakwera
Katswiri oyimba nyimbo za chamba cha Reggae, Burning Spear, wapereka gitala yake imene wakhala akuyigwiritsa ntchito kwa nthawi yayitali kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr...
Khonsolo ya BT ikumanga zikwangwani m’malire a mnzindawu
Khonsolo ya mnzinda wa Blantyre yakhazikitsa ntchito yomanga zikwangwani zodziwitsa anthu kuti akulowa kapena kutuluka munzindawu. Pokhazikitsa ntchitoyi kwa Kameza, mfumu ya mnzindawu, a Joseph...
Kalembetseni voti kuti chitukuko chipitilire — Kabwila
Ofalitsankhani kuchipani cha Malawi Congress (MCP), a Jessie Kabwila, apempha anthu m’dziko muno kuti alembetse voti m’madera mwawo pamene ntchitoyi yayamba pofuna kuti chitukuko chimene...
Chimbale chatsopano ndichothokoza Mulungu — Thuya
Oyimba nyimbo za uzimu, mayi busa Mary Thuya, ati chimbale chimene akutulutsa chotchedwa “Ndathokoza” ayimba pothokoza Mulungu kaamba kowachiritsa ku matenda a Covid-19. A Thuya...
‘Osagwiritsa ntchito ndalama za Mtukula Pakhomo ngati mkomya’
Nduna yoona kuti pasamakhale kusiyana pakati pa amayi ndi abambo, a Jean Sendeza, alangiza amayi m’dziko muno kuti asamagwiritse ntchito ndalama za Mtukula Pakhomo kuchitira...

