Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Local Local Music News Nkhani

Chimbale chatsopano ndichothokoza Mulungu — Thuya

Oyimba nyimbo za uzimu, mayi busa Mary Thuya, ati chimbale chimene akutulutsa chotchedwa “Ndathokoza” ayimba pothokoza Mulungu kaamba kowachiritsa ku matenda a Covid-19.

A Thuya anena izi pokonzekera mwambo okhazikitsa chimbalechi, umene udzakhalepo Lamulungu likudzali munzinda wa Lilongwe.

Iwo ati anthu amene adzapite kumwambowu ayembekezere kukalimbikitsika kudzera ku umboni wawo.

Oyimba ena amene akaimbe nawo ndi monga Sir Norman Phiri, Favoured Martha, Alex Nkalo, Milefa Sisters komanso Maxwell Oloto.

 

Related posts

Tiyeni tipitirize kumvera mtsogoleri komanso kukonda chipani chathu — Msukwa

Romeo Umali

Implementation of water security framework, key in addressing environmental degradation

Romeo Umali

Kalembera wa voti ali mkati

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.