Women’s Legal Resources Centre (WOLREC) has stressed the need to uphold principles of equality and inclusivity in the political arena. Maggie Banda, WOLREC’s Executive Director,...
Katswiri wampira wamiyendo wa asungwana wadziko lino, Tabitha Chawinga,amene akusewerera timu ya PSG ku France, amusankha kukhala osewera amene wakankha chikopa mododometsa mu ligi yakumeneko...
Apolisi anjata a Stanley Chirwa, amene ndi oyimira anthu pamilandu (lawyer), powaganizira kuti ali ndi galimoto la mtundu wa Ford Ranger limene lidabedwa ndi zigawenga...
Mkulu wa achinyamata m’chipani cha Malawi Congress (MCP) yemwenso ndi nduna ya maboma ang’ono, a Richard Chimwendo Banda, walangiza anthu amdera lakuzambwe m’boma la Mangochi...
Katswiri wa nkhonya m’dziko muno, Alexander ‘Cage’ Likande, wamwalira m’bandakucha wa lero pangozi ya njinga yamoto yomwe inaombana ndi galimoto. Malinga ndi zimene akunena mnzake...
Timu ya Blue Eagles, yomwe idatuluka mu ligi yaikulu chaka chatha, yayamba ulendo wake wa ligi ya m’chigawo chapakati ya Chipiku ndi chimwemwe pomwe yathambitsa...
Khonsolo ya mzinda wa Lilongwe m’mbandakucha walero wagwetsa ndi kugumula nyumba zoposa 60 zogulitsira katundu ntauni ya munzinda wa Lilongwe kamba koti eni ake anazimanga...
Malipoti akusonyeza kuti mtsogoleri wambali ya aphungu otsutsa boma kunyumba yamalamulo, a Kondwani Nankhumwa, akhazikitsa chipani chatsopano chotchedwa People’s Development Party (PDP). Malinga ndi kalata...
Apolisi ku Limbe mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi powaganizira kuti anathyola sitolo ndikuba zipangizo za galimoto, kuphatikizapo mabatire. Wachiwiri kwa ofalitsankhani zapolisi ku...