Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Akhazikitsa chipani chatsopano

Malipoti akusonyeza kuti mtsogoleri wambali ya aphungu otsutsa boma kunyumba yamalamulo, a Kondwani Nankhumwa, akhazikitsa chipani chatsopano chotchedwa People’s Development Party (PDP).

Malinga ndi kalata yomwe ayibweretsa poyera kudzera patsamba lawo la mchezo, chipanichi chichititsa msonkhano wa atolankhani posachedwapa kumenenso chidzasonyeze kumtundu wa  aMalawi atsogoleri ake ongogwirizira ma udindo.

A Nankhumwa, omwe ndi phungu wadera la pakati m’boma la Mulanje, adachotsedwa m’chipani cha Democratic Progressive (DPP) miyezi yapitayo.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Dr Chakwera apereka K5 million zothandizira pamaliro a Kasambara

Chisomo Manda

Support Public Health Services — Daudi

Foster Maulidi

Former bank teller nabbed for robbing ex-girlfriend at work

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.