Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Mussa Ajibu asambitsa chokweza Vissah

Mnyamata wadzigogodo wamdziko muno,Mussa Ajibu, lero wagonjetsa mnyamata wamtali ochokera m’dziko la South Africa, Ruan Vissah pamasewero ankhonya amene anachitikira munzinda wa Lilongwe.

Majaji onse atatu anati Ajibu ndiye wachita chamuna pamasewerowo potibula mnzakeyo.

M’masewero ena komweko, Alick Mwenda wadziko lino nayenso zake zayenda atagonjetsa Trancy Ntetu ochokera m’dziko la Canada pakutha pa ma round asanu ndi imodzi.

Related posts

Sant’Egidio launches book to promote child registration

Romeo Umali

Chitukuko chifalikira m’boma lonse la Nsanje — Zikhale

Alinafe Mlamba

Malawi to attend African Consultation Meeting for 3rd United Nations Oceans Summit

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.