Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Mussa Ajibu asambitsa chokweza Vissah

Mnyamata wadzigogodo wamdziko muno,Mussa Ajibu, lero wagonjetsa mnyamata wamtali ochokera m’dziko la South Africa, Ruan Vissah pamasewero ankhonya amene anachitikira munzinda wa Lilongwe.

Majaji onse atatu anati Ajibu ndiye wachita chamuna pamasewerowo potibula mnzakeyo.

M’masewero ena komweko, Alick Mwenda wadziko lino nayenso zake zayenda atagonjetsa Trancy Ntetu ochokera m’dziko la Canada pakutha pa ma round asanu ndi imodzi.

Related posts

CHAKWERA ARRIVES IN NEW YORK

MBC Online

Jah Prahzah, Onesimus to tussle for Artist of the Year

Romeo Umali

Japan, UN donate equipment to MBS

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.