Eunice Katunga wa ku Lunzu m’dela la Group Village Headman Kumponda mfumu yaikulu Kapeni m’boma la Blantyre wati moyo wa banja lake wasintha potsatira ntchito...
Boma ladzudzula m’chitidwe omwe anthu ena akumachita otenga ziphaso za unzika za anthu ena powanamiza kuti awamangira nyumba, mwa zina. Nduna yofalitsa nkhani, a Moses...
Bungwe la Central Region Football Association (CRFA) lapempha anthu okonda mpira wa miyendo m’dziko muno kuti abwere poyera ndikuthandiza mpira wa m’maboma. Mlembi wamkulu wa...
Bwalo lamilandu la Chief Resident Magistrate ku Lilongwe layamba laima kaye kumva mulandu omwe boma la South likufuna kuti Banja la a Bushiri lipite mdzikolo...
Unduna wazofalitsa nkhani wati ndiokhutira ndi m’mene MB ikugwirira ntchito zake pokwaniritsa zokhumba za aMalawi onse m’dziko muno. Mlembi wamkulu mu undunawu, a Baldwin Chiyamwaka,...
Akuluakulu a khonsolo ya m’boma la Nkhotakota ati kulandira kwa ndalama zachitukuko mopelewera komanso mopanda ndondomeko kukusokoneza magawo ambiri akagwiridwe kawo kantchito m’bomali. DC wa...
Apolisi ku Lilongwe amanga mwamuna wazaka 44, Patrick Zgambo, pomuganizira kuti waba zipangizo zoyimbira za ndalama pafupifupi K3.5 million za tchalitchi chotchedwa Time of God....
Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera walangiza aMalawi kuti asamamvere zonena za andale ena amene akunamiza anthu pofuna kungotchuka pa ndale chabe. A Chakwera...