K15 Million ndiyomwe ikufunika kuthandizira Peter Mlangeni
Oyimba nyimbo zauzimu amene akonza mwambo wamaimbidwe ndi cholinga chothandiza nzawo Peter Uyu Mlangeni, yemwe adavulala pangozi yagalimoto, ati pakufunika K15 Million kuti Mlangeni alandire...

