Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani Sports Sports

Wanderers idzasankha mphunzitsi watsopano gawo loyamba la super league likatha

Timu ya Mighty Mukuru Wanderers yati idzasakha mphunzitsi watsopano gawo loyamba la super league likatha ndipo yati yemwe akugwirizira udindowu Meke Mwase ali ndi mwayi waukulu otengeratu ntchitoyi.

Mwase akuthandizidwa ndi Bob Mpinganjira kutsatira ndipo adatenga udindowu pambuyo pa kutula pansi udindo kwa Nsazurwimo Ramadan.

Mkulu watimuyi, Panganeni Ndovi, wati aunikira mmene aphunzitsi ogwirizirawa agwilira ntchito gawo loyamba likatha.

Motsogozedwa ndi Mwase, timuyi yapambana masewero ake onse awiri.

Wandereres ili panambala yachitatu mu ligi ndi ma pointi 18.

By Praise Majawa

Related posts

GROW GREEN TO INVEST K720 BN IN WATER SUPPLY PROJECT

MBC Online

Quality must drive 2025 Tobacco Marketing Season – MNT

McDonald Chiwayula

Advocates call for reforms in Karonga’s mining industry

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.