Katswiri oyimba Dancehall, Malinga Mafia, wapepesa kwa okonda nyimbo zake kaamba kokanika kuyimba ku phwando lamayimbidwe la Illusionz lomwe likuchitikira pagombe m’boma la Mangochi. Katswiriyu...
Amene anajambula kanema wa Belinda, gulu la Remnant Lions, ati ali ndi chikhulupiliro kuti kanemayu alimbikitsa atsikana kuti asamafooke pa maphunziro ngakhale atakumana ndi mavuto,...
Achinyamata omwe alandira mpamba wa ndalama zokwana K1 million aliyense kuchokera kwa Triephornia Mpinganjira pansi pa ndondomeko ya ‘kuthandiza omwe alibe kuthekera kupita patsogolo’ awalangiza...
Bungwe la National Economic Empowerment Fund (NEEF) lati zomwe anthu ena akufalitsa kuti boma lakhululukira onse omwe anatenga ngongole ku NEEF kuti asabweze ndi zabodza....
Apolisi m’boma la Mangochi amanga a Smith White, 32, powaganizira kuti anaba zipangizo zomangira nyumba za K30 million ku Savijan Cottage komwe amagwirako ntchito ngati...
Anthu amene anakhudzidwa ndi ngozi ya kusefukira kwa madzi chaka chino ku Dwangwa m’boma la Nkhotakota alandira katundu osiyanasiyana wa ndalama zokwana K100 million kuchokera...
Bungwe la German Federal Bureau of Aircraft Accident Investigation (BFU) latulutsa lipoti la ngozi ya ndege imene inachitikira mu nkhalango ya Chikangawa m’boma la Mzimba,...
Achinyamata makumi atatu lero akuyembekezera kupata mwayi wa mpamba oyambira malonda okwana K1 million aliyense kuchokera kwa mayi Triephornia Mpinganjira ku BICC mu mzinda wa...
Mwambo wa misa ya maliro a malemu bambo Claude Boucher Chagomerana Chisale watha pabwalo la Kungoni m’boma la Dedza. Poyankhula, nduna yoona za malo, a...