Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Apolisi amanga mlonda pomuganizira kuti anaba

Apolisi m’boma la Mangochi amanga a Smith White, 32, powaganizira kuti anaba zipangizo zomangira nyumba za K30 million ku Savijan Cottage komwe amagwirako ntchito ngati mlonda.

Ofalitsa nkhani ku Polisi ya Mangochi, a Amina Tepani Daud, ati atachita kafukufuku anapeza kuti a White anagulitsa katunduyi yemwe amangokhala.

A Daudi ati mwini wakeyo atazindikira izi, anakanena ku polisi ndipo apolisiwo anapeza wina mwa katunduyi yemwe ndi wa ndalama zokwana K20 million.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Malawi/ Norway sign cooperation agreement to strengthen MW’s statistical system

MBC Online

MDF laments high encroachment at its training areas.

MBC Online

TIMVETSE

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.