Gulu la amayi a Zokonda Amayi a m’chigawo chakummwera lapulumuka pa ngozi ya bus imene yachitika m’boma la Ntcheu usiku wa Lachitatu. Amayiwa amachokera munzinda...
Mkulu wa bungwe la MANEPO, a Andrew Kavala, wayamikira mayi wa dziko lino, Madam Monica Chakwera, pa chidwi chawo choonetsetsa kuti achikulire m’dziko muno asamazunzidwe....
Mayi wa pfuko lino, Madam Monica Chakwera, atsegulira sukulu yatsopano ya sekondale yoyendera ya mdera la Chiyola m’boma Rumphi imene bungwe la Press Trust lamanga....
Mphunzitsi wa timu yaikulu ya mpira wa miyendo m’dziko muno, Patrick Mabedi, wati waauza anyamata ake kuti mawa adzasewere ndicholinga chofuna kubwezeretsa ulemu kudziko lino...
Timu ya Senegal yachita zokonzekera zake lero pa Bingu National Stadium, pamene ikuyembekezeka kukumana ndi timu ya Malawi mawa. Mphunzitsi wa timuyi ongogwirizira, Pape Thiaw,...
Wapampando wamwambo wa MBC Zokonda Amayi wa chaka chino, mayi Mervis Senga, ati zonse zokonzekera zamwambo wa Zokonda Amayi Macheza umene uchitikire munzinda wa Mzuzu...
Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, wati ndi udindo wa akuluakulu a boma, kuphatikizapo aku unduna oona zachilengedwe ndi kusintha kwa nyengo,...
Bungwe la Central Region Water Board (CRWB) lapereka mphoto kwa ena mwa makasitomala ake omwe amalipira madzi mokhulupirika. Cholinga cha mphotozi ndi kufuna kulimbikitsa anthu...