Malawi Broadcasting Corporation
Development Education Local Local News Nkhani

Madam Chakwera atsegula sukulu ya Chiyola CDSS

Mayi wa pfuko lino, Madam Monica Chakwera, atsegulira sukulu yatsopano ya sekondale yoyendera ya mdera la Chiyola m’boma Rumphi imene bungwe la Press Trust lamanga.

Sukuluyi ili ndi zipinda zofunika monga makalasi ophunzirira ngakhalenso chipinda chosungira mabuku.

Themba la Mathemba Chikulamayembe athokoza boma popititsa patsogolo maphunziro m’dziko muno ndipo ati chiyembekezo kuti derali litukuka kwambiri m’magawo osiyanasiyana chifukwa cha sukuluyi.

Iwo atinso atsikana mderali amayenda mtunda wautali kuti akapeze maphunziro ku sukulu za Mwasizi ngakhalenso Katowo.

Related posts

MEC reduces participation fees for women, youths in 2025 elections

Alinafe Mlamba

Madam Chakwera afika ku mwambo okumbukira tsiku la anthu achialubino

Rabson Kondowe

Seed company introduces instalments payment for farmers

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.