Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

WAIPHULA!

Mnyamata wa zaka 20  wa ku Lilongwe, wapeza mphoto ya ndalama zokwana K174.2 million  atasewera masewero oulutsa ndege ndi BetPawa.

Akuluakulu a kampaniyi atsimikiza izi ku Blantyre komwe mwambo olengeza za mnyamatayu unachitika.

Mu mbiri ya kampaniyi, yemwe anachita mphumi ndikupeza ndalama zochuluka kuposa apa ndi mkulu wina wa ku Ghana, yemwe anapeza ndalama zokwana K843 million.

Related posts

ESCOM yayamika Chakwera chifukwa cha $21 million

Romeo Umali

M’mudzi wa Kanyenda tsopano ali ndi madzi aukhondo

Alinafe Mlamba

Asiya zolemba, akufuna ku nyumba ya malamulo

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.