Nduna yoona zamphamvu zamagetsi a Ibrahim Matola yati nkofunika kuti anthu onse m’dziko muno agwirane manja popititsa patsogolo chitukuko mogwirizana ndi masomphenya a mtsogoleri wa...
Nduna zosiyanasiyana zati zambiri mwa zomwe mtsogoleri wa dziko lino, Dr. Lazarus Chakwera, analonjeza kuti zichitike mu uthenga wawo wa SONA chaka chatha, zakwaniritsidwa. Mwachitsanzo,...
Phungu wa nyumba yamalamulo wadera la kuzambwe kwa boma la Mulanje, a George Chaponda, amene awathamangitsa ku msonkhano wa akuluakulu a ku nyumba ya Malamulo...
Makhansala awiri a chipani cha Democratic Progressive (DPP) atuluka mchipanichi ndipo alowa cha Malawi Congress (MCP). Mkulu okopa anthu mu MCP a Moses Kunkuyu alandila makhansala...
Boma latsimikizila alimi mdziko muno kuti asade nkhawa za misika komwe akagulitse mbewu zao. Nduna ya zaulimi a Sam Kawale anena izi atayendela alimi omwe...
Nduna ya zachuma a Simplex Chithyola Banda ati unduna wao uonetsetsa kuti wapereka ndalama zokwanila ku bungwe la NEEF. Poyankhula pomwe akuyendela ntchito za NEEF ...
Khothi la Magistrate ku Blantyre lalamula apolisi komanso a dipatimenti ya zankhalango kuti apereke galimoto ya mtundu wa Scania yamatani 10 yomwe nambala yake ndi...