Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

CHITUKUKO CHIFIKIRE MADERA ONSE — ZIKHALE

Mmodzi wa akulu akulu mchipani cha MCP yemwenso ndi nduna yaza Chitetezo Chadziko a Ken Zikhale Ng’oma ati boma lipitiriza kutukula madera onse a dziko lino mosakondera potukula miyoyo ya anthu.

Mwachitsanzo,iwo anakamba za ntchito ya minda ikulu ikulu ya Mega Farms imene ikugwiridwa ku Machinga.

A Zikhale Ng’oma amayankhula pa bwalo laza masewero la Chaka ku Machinga pa msonkhano omwe anachititsa.

Mu kanema ali m’musiyu, akuonetsa zina zomwe a Ng’oma analankhula.

#MBCOnlineServices

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

‘Tidzibweretsa malita 2 million pa ulendo umodzi’

Beatrice Mwape

Two men nabbed over suspected intent to cause grievous harm

Romeo Umali

Mabungwe ayamika boma poyendetsa bwino chuma

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.