Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

CHITUKUKO CHIFIKIRE MADERA ONSE — ZIKHALE

Mmodzi wa akulu akulu mchipani cha MCP yemwenso ndi nduna yaza Chitetezo Chadziko a Ken Zikhale Ng’oma ati boma lipitiriza kutukula madera onse a dziko lino mosakondera potukula miyoyo ya anthu.

Mwachitsanzo,iwo anakamba za ntchito ya minda ikulu ikulu ya Mega Farms imene ikugwiridwa ku Machinga.

A Zikhale Ng’oma amayankhula pa bwalo laza masewero la Chaka ku Machinga pa msonkhano omwe anachititsa.

Mu kanema ali m’musiyu, akuonetsa zina zomwe a Ng’oma analankhula.

#MBCOnlineServices

Related posts

BUSHIRI REACHES OUT TO FOOD INSECURE FAMILIES IN LL RURAL

Rabson Kondowe

Chitipa registers more cholera cases

Romeo Umali

Alimi apeza misika ya ndalama zochuluka kuchiwonetsero chazaulimi

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.