Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Dr Chakwera achita zokambilana zobweretsa sitima zapamadzi

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera akuyembekezeka kukambirana ndi kampani zoona za sitima zapamadzi ku Germany kuti athandize kuyambitsa ntchito za maulendo pa nyanja ya Malawi pothana ndi mavuto amayendedwe panyanjayi.

Nduna yoona nkhani zakunja a Nancy Tembo anena izi pomwe Dr Chakwera akuyembekezeka kufika ku Frankfurt ku Germany lachitatu kuchokera ku Italy komwe akakambilane ndi makampaniwa.

Iwo ati ali ku Germany, Dr Chakwera akambirana ndi kampaniyi za maulendowa poonjezela kukambirana zankhani ya magetsi asanakumane ndi mtsogoleri wa dziko la Germany.

Related posts

Osewera mpira wa asungwana akusokonekera

Romeo Umali

MCP ikufuna zipani zidzichita misonkhano mwaufulu

Rabson Kondowe

DR Usi apempha NEEF iganizire aphunzitsi

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.