Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Anyamata awiri anjatidwa ataba katundu wa K500,000

Apolisi m’boma la Mangochi amanga a Rashid Mailosi a zaka 18 ndi a Paul Edward a zaka 19 powaganizira kuti anathyola nyumba yogulitsira katundu ndi kubamo katundu wandalama pafupifupi K500,000.

Ofalitsa nkhani pa polisi ya Mangochi, Amina Tepani Daudi, watsimikiza nkhaniyi ndipo wati awiriwa akaonekera kubwalo lamilandu kukayankha mulandu wakuba.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Kuli ufulu wa demokalase ku MCP— Chilondola

Mayeso Chikhadzula

RA COMMITS TO IMPROVE LL CITY ROADS

MBC Online

Dr Chakwera adzapambananso chaka chamawa – Mussa

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.