Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Anyamata awiri anjatidwa ataba katundu wa K500,000

Apolisi m’boma la Mangochi amanga a Rashid Mailosi a zaka 18 ndi a Paul Edward a zaka 19 powaganizira kuti anathyola nyumba yogulitsira katundu ndi kubamo katundu wandalama pafupifupi K500,000.

Ofalitsa nkhani pa polisi ya Mangochi, Amina Tepani Daudi, watsimikiza nkhaniyi ndipo wati awiriwa akaonekera kubwalo lamilandu kukayankha mulandu wakuba.

 

Related posts

LL Police nabs four men suspected of selling knock-off cement

Romeo Umali

LL Police hunt ESCOM transformer criminals

Romeo Umali

Mwambo wa maliro wa malemu Kayanula wayamba

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.