Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Anyamata awiri anjatidwa ataba katundu wa K500,000

Apolisi m’boma la Mangochi amanga a Rashid Mailosi a zaka 18 ndi a Paul Edward a zaka 19 powaganizira kuti anathyola nyumba yogulitsira katundu ndi kubamo katundu wandalama pafupifupi K500,000.

Ofalitsa nkhani pa polisi ya Mangochi, Amina Tepani Daudi, watsimikiza nkhaniyi ndipo wati awiriwa akaonekera kubwalo lamilandu kukayankha mulandu wakuba.

 

Related posts

National Bank yapanga phindu lokwana K71.96 billion chaka chatha

Alinafe Mlamba

Goal within reach — Tabitha

Romeo Umali

Mia wati adzapikisana nawo pampando wa wachiwiri kwa wachiwiri kwa mtsogoleri ku MCP

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.