Mlembi wamkulu wa chipani cha Malawi Congress, a Richard Chimwendo Banda, atsimikizira anthu aku Nkhotakota kuti boma lilambula msewu wa pakati pa Mwansambo m’bomalo ndi...
Boma, molumikizana ndi bungwe la UNDP, lakhazikitsa ntchito ya gawo lachiwiri komanso lachitatu ya Green Economic Transformation Facility (GETF). Ntchitoyi ikupereka danga kwa anthu komanso...
Ena mwa akatswiri oona zamalingaliro m’dziko muno ati pakufunika maphunziro ozindikiritsa ana osaposera zaka 13 momwe angadzitetezere kum’chitidwe wankhanza zogonana poyang’anira kukula kwa m’chitidwewu m’dziko...
Alimi omwe akuchita nawo ulimi wa mthilira wa minda ikuluikulu pa sikimu ya Mlambe Irrigation ku Mangochi, ayamikira bungwe la Green Belt Authority (GBA) kaamba...
Anthu a m’boma la Chiradzulu ati ndi okondwa kamba ka ntchito za chitukuko zosiyanasiyana zomwe zikuchitika kudzera mu thumba la ntchito za chitukuko laboma la...
Bungwe la National Economic Empowerment Fund (NEEF) lakhazikitsa ntchito ya ngongole yaza ulimi wa mthilira m’chigawo cha m’mphepete mwa nyanja. Mkulu wabungweli, a Humphrey Mdyetseni,...
Prezidenti wa dziko lino, Dr. Lazarus Chakwera ndi Mayi wa dziko lino, Madam Monica Chakwera, ati ndi okhudzika kwambiri ndi imfa ya mtsogoleri wa mpingo...
Bungwe la Civil Society Elections Integrity Forum ladzudzula mmodzi mwa atsogoleri a chipani cha Democratic Progressive (DPP) a Norman Chisale kaamba ka mchitidwe olankhula mau...
Anthu okhala m’mudzi mwa a Gulupu a Kaname mdera la Mfumu yayikulu Chilikumwendo m’boma la Dedza ati apindula ndi ntchito yolumikiza magetsi m’madera akumudzi ya...
Boma la United Kingdom, kudzera ku bungwe la Global Health Partnerships, lakhazikitsa ntchito yothandizo kutukula luso la anthu ogwira ntchito zaumoyo m’dziko muno. Mlembi wamkulu...