Category : Nkhani
Save The Children yapereka mbaula zamakono ku Lilongwe
Mabanja okwana makumi asanu ammudzi mwa mfumu yaikulu Masumbakhunda ozungulira khalango ya Dzalanyama m’boma la Lilongwe ali ndi chimwemwe atalandira mbaula zamakono zoyendera mphamvu ya...
Bungwe la SFFRFM lati zokonzekera AIP zili m’chimake
Bungwe la Small Holder Farmers Fertilizer Revolving Fund of Malawi (SFFRFM) lati zokonzekera zokhudza ntchito yogulitsa feteleza wotsika mtengo mundondomeko ya boma ya AIP zikuyenda...
Immigration, ACB akufuna kuthetsa ziphuphu
Bungwe la Immigration lati pakufunika mgwirizano polimbikitsa aMalawi kuti azitsata malamulo pamene akupita maiko ena. M’modzi mwa adindo ku bungweli, a Fletcher Nyirenda, anayankhula izi...
Bungwe la CARD lati MBC ndi akadaulo powulutsa mawu
Bungwe la Churches Action in Relief and Development (CARD) layamikira nyumba yowulutsa mawu ya Malawi Broadcasting Corporation (MBC) ponena kuti ndi akadaulo pantchito yawo. Mkulu...
Kabaza operators urged to comply with road traffic regulation
Dedza Police Traffic Section Head Inspector Finai Mwaighogha has challenged motorbike-taxi operators to adhere to road traffic rules to reduce road accidents in Dedza District....
‘Nyumba yamalamulo ya ana ikufunika thumba lapadera’
Komiti ya kunyumba ya malamulo yowona za chisamaliro cha anthu yati dziko lino likufunika thumba lapadera loyendetsera mikumano komanso ntchito za nyumba yamalamulo ya ana...

