Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Politics

Khamu lakonzeka kumva mfundo za chitukuko ku Lilongwe

Anthu ochuluka akhamukira ku bwalo lamasewero la pa msika wa Area 24 ku Lilongwe komwe kukhale msonkhano wa chipani cha Malawi Congress (MCP).

Pakadali pano, zokonzekera zonse zatha pamene anthu akudikira mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera kuti adzakhale nawo pa msonkhanowu.

Magule osiyanasiyana akuvinidwaa ndipo oyimba monga Skeffa Chimoto komanso Mlaka Maliro akusangalatsa anthu.

Akuluakulu achipani, aphungu anyumba yamalamulo, mafumu a m’boma la Lilongwe, anyamata, asungwana komanso amayi ndi abambo adzadza pa bwalo la Maseweroli.

Related posts

Retired nurse assisted after appearing on Reach Out and Touch

Rabson Kondowe

Bwaila Fistula Centre calls for support to treat more fistula patients

Romeo Umali

Chakwera receives 2024 National Projects

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.