Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Politics

Khamu lakonzeka kumva mfundo za chitukuko ku Lilongwe

Anthu ochuluka akhamukira ku bwalo lamasewero la pa msika wa Area 24 ku Lilongwe komwe kukhale msonkhano wa chipani cha Malawi Congress (MCP).

Pakadali pano, zokonzekera zonse zatha pamene anthu akudikira mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera kuti adzakhale nawo pa msonkhanowu.

Magule osiyanasiyana akuvinidwaa ndipo oyimba monga Skeffa Chimoto komanso Mlaka Maliro akusangalatsa anthu.

Akuluakulu achipani, aphungu anyumba yamalamulo, mafumu a m’boma la Lilongwe, anyamata, asungwana komanso amayi ndi abambo adzadza pa bwalo la Maseweroli.

Related posts

LoS returns

Rabson Kondowe

Likoma District Council budget now at K3.9 billion

Romeo Umali

ALLAN WITTIKA’S MURDER CASE REFERRED TO HIGH COURT

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.