Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Politics

Khamu lakonzeka kumva mfundo za chitukuko ku Lilongwe

Anthu ochuluka akhamukira ku bwalo lamasewero la pa msika wa Area 24 ku Lilongwe komwe kukhale msonkhano wa chipani cha Malawi Congress (MCP).

Pakadali pano, zokonzekera zonse zatha pamene anthu akudikira mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera kuti adzakhale nawo pa msonkhanowu.

Magule osiyanasiyana akuvinidwaa ndipo oyimba monga Skeffa Chimoto komanso Mlaka Maliro akusangalatsa anthu.

Akuluakulu achipani, aphungu anyumba yamalamulo, mafumu a m’boma la Lilongwe, anyamata, asungwana komanso amayi ndi abambo adzadza pa bwalo la Maseweroli.

Related posts

Chakwera visits Kamuzu Tree in Chikangawa

Romeo Umali

Salima Sugar makes K2.4 billion profit

Yamikani Simtowe

Court convicts two women for selling Gentamicin as HIV cure

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.