Category : Nkhani
Ntchito yopopa madzi mu nyanja ya Malawi ichepetsa vuto la madzi ku Dowa – Chakwera
Prezidenti wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera watsimikizira anthu m’boma la Dowa kuti ntchito yopopa madzi m’nyanja ya Malawi ithandiza kubweretsa ukhondo ndi madzi pafupi...
Mfumu yaikulu Mkukula yayamika boma kaamba ka chitukuko cha madzi ammipopi
Mfumu yaikulu Mkukula ya m’boma la Dowa yayamika boma chifukwa chowapatsa anthu akwa Mkukula chitukuko cha madzi a m’mipopi. Mfumuyi yati m’mbuyomu anthu mderali amavutikira...
Wobera anthu m’magalimoto amugamula zaka zitatu kundende
Bwalo la milandu la First Grade Magistrate ku Karonga lagamula a Mussa Banda kuti akakhale kundende kwazaka zitatu ndikugwira ntchito yakalavula gaga chifukwa chopezeka olakwa...
Tithandizeni kuthana ndi ngongole – Mzuzu City Council
Khonsolo ya mnzinda wa Mzuzu yapempha komiti yakunyumba yamalamulo yoona momwe chuma chaboma chikugwilira ntchito ya Public Accounts Committee kuti ithandizirepo pamavuto angapo omwe khonsoloyi...
Mvula yamphamvu yaononga katundu ku Mangochi
Katundu yemwe bungwe la Malawi Council for Disability Affairs (MACODA) limayenera kugawa kwa anthu ovutika mdera la Mtanga kwa mfumu yaikulu Chimwala Ku Mangochi wakokoloka...
Boma lagawa chimanga ku Zomba
Boma lakhazikitsa ntchito yogawa chimanga kwa mabanja pafupifupi 8000 amene njala inawakhudza munzinda wa Zomba. Mwambo okhazikitsa ntchitoyi unachitika Lachitatu ku Matawale kwa mfumu yayikulu...
Kalembera wa voti ali mkati
Ntchito yolemba mayina a anthu m’kaundula wa voti ili mkati pa sukulu ya pulayimare ya Manja ku Blantyre. Pamene MBC inayendera pa malowa inapeza kuti...
Mfumu Ngokwe yayamika magulu akufuna kwabwino
Mfumu yayikulu Ngokwe m’boma la Machinga yayamikira ntchito imene magulu ena, kuphatikizapo atsogoleri azipembedzo, akugwira pofikira mabanja amene akukumana ndi vuto la kusowa kwa chakudya....

