Malawi Broadcasting Corporation
Culture Local News Nkhani Politics

‘Enock Chihana apepese’

Bungwe la Chewa Heritage Malawi – Chifukwato cha a Chewa lauza a Enock Chihana kuti apepese mtundu wa a Chewa pazimene adayankhula pamsonkhano wa olembankhani Lachitatu munzinda wa Lilongwe.

Iwo ati a Chihana adayankhula mawu achipongwe pa msonkhanowo.

Wapampando wa bungweli, Mfumu Sosola, ati bungwe lawo lapereka masiku atatu kwa a Chihana kuti apepese kupanda kutero adzawaitana kuti akawaonetse kudambwe.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

ECM condemns assault on Catholic nun

MBC Online

E-payments in Mtukula Pakhomo excites beneficiaries

MBC Online

Inhouse media signs Keli P

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.