Kampani ya Nkhokwe Fertilizer Limited yapempha boma kuti liganizire zoyika feteleza wawo pa ndondomeko ya zipangizo zotsika mtengo za AIP chifukwa ali ndi kuthekera kobwezeretsa...
Thupi la amene anali mkhalakale pa nkhani zoulutsa mawu, Joshua Kambwiri, alitengera ku mudzi kwawo ku Domasi m’boma la Zomba, kumene akaliyike m’manda mawa Lolemba....
Boma lati anthu okhala komanso ochita malonda kufupi ndi njanji ali ndi udindo oteteza zipangizo za njanji kuti ntchito za sitima zipite patsogolo m’dziko muno....
Traditional leaders in Dowa have assured President Dr Lazarus Chakwera of a landslide victory in the district because of developments he is implementing nationwide. Senior...
Matimu 24 amu chikho cha Tambala Super cha m’boma la Blantyre alandira ndalama zawo kuchokera kwa othandiza chikhochi a Amazon Group of Companies. Awa ndi...
Mafumu andodo, pansi pa bungwe lawo la Chewa Heritage Foundation (CHEFO), ati udindo waukulu wa bungwelo ndi kupititsa patsogolo, kuteteza ndi kusunga chikhalidwe ndi miyambo...