Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Kambwiri ayikidwa mmanda mawa

Thupi la amene anali mkhalakale pa nkhani zoulutsa mawu, Joshua Kambwiri, alitengera ku mudzi kwawo ku Domasi m’boma la Zomba, kumene akaliyike m’manda mawa Lolemba.

Mwambo wa mapemphero otsanzikana ndi malemu Kambwiri unachitikira pa tchalitchi cha Ngumbe CCAP ku Chileka munzinda wa Blantyre kumene malemuwa amapemphera.

Malemu Kambwiri, amene anagwirapo ntchito ku nyumba youlutsa mawu ya MBC, amwalira ali ndi zaka 62.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

163,000 candidates to write JCE this year

Chisomo Break

Boma lilimbikitsa sukulu za Kwacha

Beatrice Mwape

MANEPO’s UK Aid Match Project facilitates more than 6,000 eye surgeries

Paul Mlowoka
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.